1
Eksodo 14:14
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Yehova adzakumenyerani nkhondo. Inu mungokhala chete.”
ತಾಳೆಮಾಡಿ
Eksodo 14:14 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
2
Eksodo 14:13
Mose anayankha anthu kuti, “Musachite mantha. Imani, ndipo muone chipulumutso chimene Yehova akuchitireni lero. Aigupto amene mukuwaona lerowa simudzawaonanso.
Eksodo 14:13 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
3
Eksodo 14:16
Nyamula ndodo yako ndi kutambasula dzanja lako kuloza ku nyanja, kugawa madzi kuti Aisraeli awoloke powuma.
Eksodo 14:16 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
4
Eksodo 14:31
Choncho Aisraeli anaona dzanja lamphamvu la Yehova limene linagonjetsa Aigupto aja, ndipo iwo anaopa Yehova ndi kumukhulupirira pamodzi ndi mtumiki wake Mose.
Eksodo 14:31 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ