1
Eksodo 1:17
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Koma azambawo ankaopa Mulungu ndipo sanachite zimene mfumu ya Igupto inawawuza kuti achite. Iwo analeka ana aamuna kuti akhale ndi moyo.
ತಾಳೆಮಾಡಿ
Eksodo 1:17 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
2
Eksodo 1:12
Koma pamene ankawazunza kwambiri, Aisraeli ndiye ankachulukirachulukira mpaka kubalalikira mʼdziko lonse. Kotero Aigupto anayamba kuopa Aisraeliwo
Eksodo 1:12 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
3
Eksodo 1:21
Pakuti azambawo ankaopa Mulungu, Iye anawapatsa mabanja awoawo.
Eksodo 1:21 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
4
Eksodo 1:8
Pambuyo pake mfumu yatsopano imene sinkamudziwa Yosefe, inayamba kulamulira dziko la Igupto.
Eksodo 1:8 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ