YouVersion Logo
ბიბლიაგეგმებივიდეოები
Get the app
Language Selector
Search Icon

Popular Bible Verses from Gen. 4

1

Gen. 4:7

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Ukadachita zabwino, ndikadakondwera nawe. Koma chifukwa choti wachita zoipa, tchimo lakukhalirira pa khomo ngati chilombo cholusa. Likulakalaka kuti likugwire, koma iweyo uligonjetse tchimolo.”

Compare

Explore Gen. 4:7

2

Gen. 4:26

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Seti adabereka mwana namutcha Enosi. Nthaŵi imeneyo anthu adayamba kutama dzina la Chauta mopemba.

Compare

Explore Gen. 4:26

3

Gen. 4:9

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Tsono Chauta adafunsa Kainiyo kuti, “Kodi mng'ono wako Abele ali kuti?” Iye adayankha kuti, “Sindikudziŵa. Kodi ndi ntchito yanga kusamala mng'ono wangayo?”

Compare

Explore Gen. 4:9

4

Gen. 4:10

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Chauta adamufunsanso kuti, “Kodi wachita chiyani? Magazi a mng'ono wako akulira kwa Ine kuchokera m'nthaka.

Compare

Explore Gen. 4:10

5

Gen. 4:15

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Koma Chauta adamuyankha kuti, “Iyai, aliyense wopha iwe Kaini adzalangidwa, ndipo Ineyo ndidzamulipsira kasanunkaŵiri.” Motero Chauta adaika chizindikiro pa Kaini kuchenjeza aliyense kuti asamuphe Kainiyo.

Compare

Explore Gen. 4:15

Free Reading Plans and Devotionals related to Gen. 4

Previous Chapter
Next Chapter
YouVersion

Encouraging and challenging you to seek intimacy with God every day.

Ministry

შესახებ

Careers

მოხალისე

Blog

Press

Useful Links

Help

დახმარება

Bible Versions

აუდიო ბიბლიები

Bible Languages

Verse of the Day


A Digital Ministry of

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

კონფიდენციალურობის წესდებაTerms
Vulnerability Disclosure Program
ფეისბუქიტვიტერზეინსტაგრამიYouTubePinterest

მთავარი

ბიბლია

გეგმები

ვიდეოები