Logo YouVersion
Icona Cerca

GENESIS 26:4-5

GENESIS 26:4-5 BLP-2018

ndipo ndidzachulukitsa mbeu zako monga nyenyezi za kumwamba, ndipo ndidzapatsa mbeu zako maiko onsewa; m'mbeu zako mitundu yonse ya dziko lapansi idzadalitsidwa; chifukwa kuti Abrahamu anamvera mau anga, nasunga chilangizo changa, ndi maweruziro anga, ndi malemba anga ndi malamulo anga.

Video per GENESIS 26:4-5

Piani di Lettura e Devozionali gratuiti relativi a GENESIS 26:4-5