1
Maluko 4:39-40
Nyanja
NTNYBL2025
Ndiipo Yesu wadauka ni kuunyindila mwela, “Khala chete!” Pampajha mwela udasiya ni nyanja idagona. Chimwecho Yesu wadaakambila oyaluzidwa wake, “Ndande yanji muopa? Bwanji, mkali mlibe chikulupililo?”
Lee anya n'etiti ihe abụọ
Nyochaa Maluko 4:39-40
2
Maluko 4:41
Oyaluzidwa wake adaopa kupunda, adafunjhana, “Mundhu wa mtundu wanji uyu mbaka mwela umvela?”
Nyochaa Maluko 4:41
3
Maluko 4:38
Yesu wadali kumbuyo kwa lijha boti wadatogonela philo, oyaluzidwa wake adamuucha ni kumkambila, “Oyaluza, simganizila kuti ife titobila?”
Nyochaa Maluko 4:38
4
Maluko 4:24
Chinchijha wadaakambila, “Mkhale maso ni yayo muyavela. Chimchijha umo mujhichocha kuvechela mawu nde chimwecho Mnungu siwakuchite ulijhiwe mawu kupunda.
Nyochaa Maluko 4:24
5
Maluko 4:26-27
Yesu wadaendekela kukamba, “Ufumu wa Mnungu ulingati chimwechi. Mundhu mmojhi wadamijha mbewu mmunda. Usiku wamagona, ni usana wakhala maso, mbeu zimela ni kukula popande iye siwajhiwa icho chichitika.
Nyochaa Maluko 4:26-27
6
Maluko 4:23
Mchate icho mkambidwa!”
Nyochaa Maluko 4:23
Ebe Mmepe Nke Mbụ Nke Ngwá
Akwụkwọ Nsọ
Atụmatụ Ihe Ogụgụ Gasị
Vidiyo Gasị