1
Maluko 2:17
Nyanja
NTNYBL2025
Yesu yapo wadavela yameneyo, wadaayangha, “Wandhu yawo sadwala siafuna sing'anga, nambho anyiawo afuna sing'anga nianyiwajha adwala. Sinidajhe kwatana wandhu yawo avomelezeka pamaso pa Mnungu, nambho najha kwatana amachimo.”
Lee anya n'etiti ihe abụọ
Nyochaa Maluko 2:17
2
Maluko 2:5
Yesu yapo wadaona chikhulupililo chao, wadamkambila yujha mundhu wovuwala, “Bwenji langa, nakulekelela machimo yako.”
Nyochaa Maluko 2:5
3
Maluko 2:27
Ndiipo Yesu wadaakambila, “Siku lo Pumulila lidaikidwa ndande ya kwathangatila wandhu, ni osati kwachita wandhu akhale akapolo a siku!
Nyochaa Maluko 2:27
4
Maluko 2:4
Saadakhoze kumpeleka pafupi ni Yesu ndande ya lijha gulu la wandhu. Chimwecho adakwela pamwamba, adafulumula chindu, pajha wadali Yesu. Yapo adafulumula, adamchicha mundhu yujha uku amgoneka pa chitala.
Nyochaa Maluko 2:4
5
Maluko 2:10-11
Chipano, nifuna mjhiwe kuti ine Mwana wa Mundhu nali ni ulamulilo wolekelela machimo ya wandhu pajhiko.” Pamenepo, wadamkambila yujha mundhu wadavuwala, “Nikukambila, uka utenge chitala chako, upite kukhomo!”
Nyochaa Maluko 2:10-11
6
Maluko 2:9
Nichiti chili chopepuka kupunda, kumkambila mundhu uyu wavuwala, ‘Walekeledwa machimo yako,’ kapina kumkambila, ‘Uka, utenge chitala chako upite?’
Nyochaa Maluko 2:9
7
Maluko 2:12
Pampajha yujha wodwala wadauka, wadatenga chitala chake ni kuchoka, uku wandhu wonjhe niampenya. Wandhu wonjhe adazizwa ni kumtamanda Mnungu, niakamba, “Sitidaonepo chindhu ngati ichi.”
Nyochaa Maluko 2:12
Ebe Mmepe Nke Mbụ Nke Ngwá
Akwụkwọ Nsọ
Atụmatụ Ihe Ogụgụ Gasị
Vidiyo Gasị