1
Matayo 17:20
Nyanja
NTNYBL2025
Yesu wadaayangha, “Ndande ya chikhulupi chanu chochepa. Nikukambilani uzene, ngati mdakakhala ni chikulupi ngati mbeu ya aladali, mdakakhoza kulikambila phili ili, ‘Chokapo upite yapo’ nalo udakapita. Palibe chindhu icho sichilepeleke kwanu.
Lee anya n'etiti ihe abụọ
Nyochaa Matayo 17:20
2
Matayo 17:5
Petulo yapo wamakamba chimwecho, mtambo wong'azikila udavinikila, ni mvekelo udaveka kuchoka kumtambo, “Uyu nde Mwana wanga uyo nimkonda, nikondwela nayo kupunda, mveleni iye.”
Nyochaa Matayo 17:5
3
Matayo 17:17-18
Yesu wadaayangha, “Imwe mbadwa wopande chikhulupi ni olakwa! Sinikhale ni anyiimwe mbaka liti? Sinikulimbileni mtima mbaka liti? Jhinayoni pano mnyamatayo.” Ndiipo Yesu wadachinyindila chiwanda, nacho chidamchoka mnyamata, ni wadalama pampajha.
Nyochaa Matayo 17:17-18
Ebe Mmepe Nke Mbụ Nke Ngwá
Akwụkwọ Nsọ
Atụmatụ Ihe Ogụgụ Gasị
Vidiyo Gasị