Logo YouVersion
BibPlan yoVideyo
Pran aplikasyon an
Seleksyone Lang
Chache Icon

Vèsè popilè nan Bib la ki soti nan AROMA 11

1

AROMA 11:36

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Chifukwa zinthu zonse zichokera kwa Iye, zichitika mwa Iye, ndi kufikira kwa Iye. Kwa Iyeyo ukhale ulemerero kunthawi zonse. Amen.

Konpare

Eksplore AROMA 11:36

2

AROMA 11:33

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ha! Kuya kwake kwa kulemera ndi kwa nzeru ndi kwa kudziwa kwake kwa Mulungu! Osasanthulikadi maweruzo ake, ndi njira zake nzosalondoleka!

Konpare

Eksplore AROMA 11:33

3

AROMA 11:34

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Pakuti anadziwitsa ndani mtima wake wa Ambuye? Kapena anakhala mphungu wake ndani?

Konpare

Eksplore AROMA 11:34

4

AROMA 11:5-6

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Choteronso nthawi yatsopano chilipo chotsalira monga mwa kusankha kwa chisomo. Koma ngati kuli ndi chisomo, sikulinso ndi ntchito ai; ndipo pakapanda kutero, chisomo sichikhalanso chisomo.

Konpare

Eksplore AROMA 11:5-6

5

AROMA 11:17-18

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Koma ngati nthambi zina zinathyoledwa, ndipo iwe, ndiwe mtengo wa azitona wa kuthengo, unalumikizidwa mwa izo, nugawana nazo za muzu za mafuta ake a mtengowo, usadzitama iwe wekha pa nthambizo: koma ngati udzitama wekha, suli iwe amene unyamula muzu, ai, koma muzu ukunyamula iwetu.

Konpare

Eksplore AROMA 11:17-18

Plan lekti ak devosyon gratis yo ki gen rapò ak AROMA 11

Chapit Avan yo
Chapit suivan
YouVersion

Ankouraje ak defi pou w chèche entimite ak Bondye chak jou.

Ministè

Apwopo

Karyè yo

Volontè

Blòg

Peze

Lyen itil yo

Ed

Fè yon don

Vèsyon Bib yo

Odyo Bib yo

Diferan Lang yo nan Bib la

Vèsè Jodi a


Yon Ministè Digital nan

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Politik PriveTèm yo
Pwogram Divilgasyon Vilnerabilite
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Akèy

Bib

Plan yo

Videyo