YouVersion Logo
બાઇબલયોજનાઓવિડિઓઝ
Get the app
Language Selector
Search Icon

Popular Bible Verses from Matayo 22

1

Matayo 22:37-39

Nyanja

NTNYBL2025

Yesu wadamuyangha, “Mkonde Ambuye Mnungu wako kwa mtima wako onjhe ni mzimu wako onjhe ni njelu zako zonjhe. Ili nde lamulo lalikulu ni loyamba. Lamulo la kawili lilingana ni ili, ‘Mkonde mnjako ngati umo ujhikondela umwene wake.’

Compare

Matayo 22:37-39 ખોજ કરો

2

Matayo 22:40

Nyanja

NTNYBL2025

Pamathuko yonjhe ni mayaluzo ya alosi, yonjhe yachokana ni malamulo yaya yawili.”

Compare

Matayo 22:40 ખોજ કરો

3

Matayo 22:14

Nyanja

NTNYBL2025

Yesu wadamaliza kwa kukamba, “Wandhu yawo alalikidwa ni ambili, nambho yawo asanghidwa ni ochepa.”

Compare

Matayo 22:14 ખોજ કરો

4

Matayo 22:30

Nyanja

NTNYBL2025

Wandhu yapo ahyuka palibe kukwata kapena kukwatiwa, siakhale ngati mtumiki wa kumwamba.

Compare

Matayo 22:30 ખોજ કરો

5

Matayo 22:19-21

Nyanja

NTNYBL2025

Nilangizeni gelenjha la ndalama iyo mlipila msongho!” Anyiiwo adampelekela gelenjha la ndalama. Ndiipo Yesu wadafunjha, “Bwanji, nghope ni jhina ili ni vayani?” Adamuyangha, “Va mfumu wa ku Loma,” Pamwepo Yesu wadakambila, “Va mfumu wa ku Loma mpacheni mfumu wa ku Loma ni va Amnungu mpacheni Mnungu.”

Compare

Matayo 22:19-21 ખોજ કરો

મફત વાંચન યોજનાઓ અને Matayo 22થી સંબંધિત મનન

Previous Chapter
Next Chapter
યુવર્ઝન

Encouraging and challenging you to seek intimacy with God every day.

Ministry

વિષે

Careers

સ્વયંસેવક

બ્લોગ

દબાવો

Useful Links

સહાય કરો

દાન કરો

બાઇબલ આવૃત્તિઓ

ઑડિયો બાઇબલ

Bible Languages

આજનું વચન


A Digital Ministry of

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

ગોપનીયતા નીતિશરતો
Vulnerability Disclosure Program
ફેસબુકટ્વીટરઇન્સ્ટાગ્રામYouTubePinterest

હોમ

બાઇબલ

યોજનાઓ

વિડિઓઝ