YouVersion Logo
બાઇબલયોજનાઓવિડિઓઝ
Get the app
Language Selector
Search Icon

Popular Bible Verses from Matayo 2

1

Matayo 2:11

Nyanja

NTNYBL2025

Ndiipo adalowa mnyumba ni adamuona mwana pamojhi ni Maliya maye wake. Adagwada ni kumlambila. Adamasula mbhaso zao ni kumpacha mwana zaabu ni ubani ni mnghwala uwo utanidwa manemane.

Compare

Matayo 2:11 ખોજ કરો

2

Matayo 2:1-2

Nyanja

NTNYBL2025

Yesu wadabadwa ku mujhi wa Beselehemu mjhiko la Yudea. Ndhawi imeneyo Helode wadali mfumu. Yesu yapo wadandobadwa wandhu yawo amajhiwa icho sichichokele adafika ku Yelusalemu adaafunjha, “Walikuti mwana uyo wabadwa Mfumu wa Ayahudi? Pakuti tayiona ndhondwa yake kudela la kumwela ni nafenjho tajha kumulambila.”

Compare

Matayo 2:1-2 ખોજ કરો

3

Matayo 2:10

Nyanja

NTNYBL2025

Yapo adaiona ndhondwa ijha adakondwa kupunda.

Compare

Matayo 2:10 ખોજ કરો

4

Matayo 2:12-13

Nyanja

NTNYBL2025

Ndiipo Mnungu adaonya kumaloto kuti asadabwelela kwa Helode. Chimwecho adabwela kujhiko lawo kwa kupitila njila yina. Wandhu yapo adatochoka mtumiki wa Ambuye wadamujhela Yusufu kumaloto ni kumkambila kuti, “Nyamuka umutenge mwana ni maye wake mthawile Kumisili. Mkakhale kumweko mbaka yapo sinikukambile pakuti Helode wafuna kuti wamphe mwanayo.”

Compare

Matayo 2:12-13 ખોજ કરો

મફત વાંચન યોજનાઓ અને Matayo 2થી સંબંધિત મનન

Previous Chapter
Next Chapter
યુવર્ઝન

Encouraging and challenging you to seek intimacy with God every day.

Ministry

વિષે

Careers

સ્વયંસેવક

બ્લોગ

દબાવો

Useful Links

સહાય કરો

દાન કરો

બાઇબલ આવૃત્તિઓ

ઑડિયો બાઇબલ

Bible Languages

આજનું વચન


A Digital Ministry of

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

ગોપનીયતા નીતિશરતો
Vulnerability Disclosure Program
ફેસબુકટ્વીટરઇન્સ્ટાગ્રામYouTubePinterest

હોમ

બાઇબલ

યોજનાઓ

વિડિઓઝ