1
Matayo 11:28
Nyanja
NTNYBL2025
“Majhani kwa ine, mwaonjhe mchauchika ni kuvutika ni makatundu yolemela, ine sinikuchiteni mpumulile.
Compare
Matayo 11:28 ખોજ કરો
2
Matayo 11:29
Jhichocheni kwa ine ni mnitumikile, mujhiyaluze kwanga, pakuti ine asati okalipa ni nilibe mbuli, namwenjho simpumulile.
Matayo 11:29 ખોજ કરો
3
Matayo 11:30
Pakuti, mayaluzo yayo nikupachani asati yolimba ni yopepuka.”
Matayo 11:30 ખોજ કરો
4
Matayo 11:27
“Atate wanga anipacha vindu vonjhe. Palibe uyo wamjhiwa Mwana nambho Tate wakepe, ni walionjhe yujha Mwana wamsangha kumvunukulila kuti waajhiwe Atate.”
Matayo 11:27 ખોજ કરો
5
Matayo 11:4-5
Yesu wadaayangha, “Pitani ni mkamkambile Yohana yayo mwayaona ni kuyavela. Osapenya apenya, viwete ayenda, amakate alamichidwa, osavela avela, akufa ahyukichidwa ni osauka alalikidwa Uthenga wa Bwino.
Matayo 11:4-5 ખોજ કરો
6
Matayo 11:15
Uyo wali nimakutu yovela, wavele!”
Matayo 11:15 ખોજ કરો
હોમ
બાઇબલ
યોજનાઓ
વિડિઓઝ