1
Genesis 16:13
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Hagara anatcha Yehova amene anamuyankhula uja dzina loti: “Ndinu Mulungu amene mumandiona,” popeza anati, “Ndakumana ndi Yehova atatha kundikomera mtima.”
Compare
Genesis 16:13 ખોજ કરો
2
Genesis 16:11
Mngelo wa Yehova uja anamuwuzanso kuti, “Ndiwe woyembekezera ndipo udzabala mwana wamwamuna. Udzamutcha dzina lake Ismaeli, pakuti Yehova wamva kulira chifukwa cha kuzunzika kwako.
Genesis 16:11 ખોજ કરો
3
Genesis 16:12
Iye adzakhala munthu wa khalidwe ngati mʼmbulu wamisala; adzadana ndi aliyense ndipo anthu onse adzadana naye, adzakhala mwaudani pakati pa abale ake onse.”
Genesis 16:12 ખોજ કરો
હોમ
બાઇબલ
યોજનાઓ
વિડિઓઝ