1
1 AKORINTO 3:16
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Kodi simudziwa kuti muli Kachisi wa Mulungu, ndi kuti Mzimu wa Mulungu agonera mwa inu?
Comparar
Explorar 1 AKORINTO 3:16
2
1 AKORINTO 3:11
Pakuti palibe munthu akhoza kuika maziko ena, koma amene aikidwako, ndiwo Yesu Khristu.
Explorar 1 AKORINTO 3:11
3
1 AKORINTO 3:7
Chotero sali kanthu kapena wookayo, kapena wothirirayo; koma Mulungu amene akulitsa.
Explorar 1 AKORINTO 3:7
4
1 AKORINTO 3:9
Pakuti ife ndife antchito anzake a Mulungu; chilimo cha Mulungu, chimango cha Mulungu ndi inu.
Explorar 1 AKORINTO 3:9
5
1 AKORINTO 3:13
ntchito ya yense idzaonetsedwa; pakuti tsikulo lidzaisonyeza, chifukwa kuti yavumbululuka m'moto; ndipo moto wokha udzayesera ntchito ya yense ikhala yotani.
Explorar 1 AKORINTO 3:13
6
1 AKORINTO 3:8
Koma wookayo ndi wothirirayo ali amodzi; koma yense adzalandira mphotho yake ya iye yekha, monga mwa kuchititsa kwake kwa iye yekha.
Explorar 1 AKORINTO 3:8
7
1 AKORINTO 3:18
Munthu asadzinyenge yekha; ngati wina ayesa kuti ali wanzeru mwa inu m'nthawi yino ya pansi pano, akhale wopusa, kuti akakhale wanzeru.
Explorar 1 AKORINTO 3:18
Inicio
Biblia
Planes
Vídeos