1
LEVITIKO 19:18
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Usamabwezera chilango, kapena kusunga kanthu kukhosi pa ana a anthu a mtundu wako; koma uzikonda mnansi wako monga udzikonda wekha; Ine ndine Yehova.
Porovnat
Zkoumat LEVITIKO 19:18
2
LEVITIKO 19:28
Musamadzicheka matupi anu chifukwa cha akufa, kapena kutema mphini; Ine ndine Yehova.
Zkoumat LEVITIKO 19:28
3
LEVITIKO 19:2
Nena ndi khamu lonse la ana a Israele, nuti nao, Muzikhala oyera; pakuti Ine ndine Yehova Mulungu wanu, ndine woyera.
Zkoumat LEVITIKO 19:2
4
LEVITIKO 19:17
Usamamuda mbale wako mumtima mwako; umdzudzule munthu mnzako ndithu, usadzitengera uchimo chifukwa cha iye.
Zkoumat LEVITIKO 19:17
5
LEVITIKO 19:31
Musamatembenukira kwa obwebweta, kapena anyanga; musawafuna, ndi kudetsedwa nao; Ine ndine Yehova Mulungu wanu.
Zkoumat LEVITIKO 19:31
6
LEVITIKO 19:16
Usamayendayenda nusinjirira mwa anthu a mtundu wako; usamatsata mwazi wa mnansi wako; Ine ndine Yehova.
Zkoumat LEVITIKO 19:16
Domů
Bible
Plány
Videa