1
EKSODO 13:21-22
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Ndipo Yehova anawatsogolera usana ndi mtambo njo kuwatsogolera m'njira; ndi usiku ndi moto njo, wakuwawalitsira; kuti ayende usana ndi usiku; sanachotse mtambo usana, kapena mtambo wamoto usiku, pamaso pa anthu.
Porovnat
Zkoumat EKSODO 13:21-22
2
EKSODO 13:17
Ndipo kunakhala pamene Farao adalola anthu amuke, Mulungu sanawatsogolere njira ya dziko la Afilisti, ndiyo yaifupi; pakuti Mulungu anati, Angadodome anthuwo pakuona nkhondo ndi kubwerera m'mbuyo kunka ku Ejipito.
Zkoumat EKSODO 13:17
3
EKSODO 13:18
Koma Mulungu anawazungulitsa anthuwo, ku njira ya kuchipululu ya Nyanja Yofiira; ndipo ana a Israele anakwera kuchokera m'dziko la Ejipito okonzeka.
Zkoumat EKSODO 13:18
Domů
Bible
Plány
Videa