1
Mateyu 9:37-38
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Pamenepo anati kwa ophunzira ake, “Zokolola ndi zambiri koma antchito ndi ochepa. Nʼchifukwa chake, pemphani Ambuye mwini zokolola kuti atumize antchito ku munda wake.”
Compara
Explorar Mateyu 9:37-38
2
Mateyu 9:13
Koma pitani kaphunzireni tanthauzo la mawu awa: ‘Ndimafuna chifundo osati nsembe ayi.’ Pakuti sindinabwere kudzayitana olungama koma ochimwa.”
Explorar Mateyu 9:13
3
Mateyu 9:36
Ataona maguluwo, anagwidwa ndi chisoni chifukwa anali ozunzika ndi osowa chithandizo ngati nkhosa zopanda mʼbusa.
Explorar Mateyu 9:36
4
Mateyu 9:12
Yesu atamva, anati, “Munthu wamoyo safuna singʼanga ayi, koma wodwala.
Explorar Mateyu 9:12
5
Mateyu 9:35
Yesu anayendayenda mʼmizinda yonse ndi mʼmidzi, kuphunzitsa mʼmasunagoge awo, nalalikira Uthenga Wabwino wa ufumu ndi kuchiritsa nthenda zawo zonse ndi zofowoka za mʼmatupi mwawo.
Explorar Mateyu 9:35