Logotip de YouVersion
La BíbliaPlansVídeos
Aconsegueix l'aplicació
Selector d'idiomes
Icona de cerca

Versets bíblics populars de Mateyu 9

1

Mateyu 9:37-38

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Pamenepo anati kwa ophunzira ake, “Zokolola ndi zambiri koma antchito ndi ochepa. Nʼchifukwa chake, pemphani Ambuye mwini zokolola kuti atumize antchito ku munda wake.”

Compara

Explorar Mateyu 9:37-38

2

Mateyu 9:13

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Koma pitani kaphunzireni tanthauzo la mawu awa: ‘Ndimafuna chifundo osati nsembe ayi.’ Pakuti sindinabwere kudzayitana olungama koma ochimwa.”

Compara

Explorar Mateyu 9:13

3

Mateyu 9:36

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Ataona maguluwo, anagwidwa ndi chisoni chifukwa anali ozunzika ndi osowa chithandizo ngati nkhosa zopanda mʼbusa.

Compara

Explorar Mateyu 9:36

4

Mateyu 9:12

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Yesu atamva, anati, “Munthu wamoyo safuna singʼanga ayi, koma wodwala.

Compara

Explorar Mateyu 9:12

5

Mateyu 9:35

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Yesu anayendayenda mʼmizinda yonse ndi mʼmidzi, kuphunzitsa mʼmasunagoge awo, nalalikira Uthenga Wabwino wa ufumu ndi kuchiritsa nthenda zawo zonse ndi zofowoka za mʼmatupi mwawo.

Compara

Explorar Mateyu 9:35

Plans de lectura i devocionals gratuïts relacionats amb Mateyu 9

Capítol anterior
Capítol següent
YouVersion

Animant-te i desafiant-te a buscar la intimitat amb Déu cada dia.

Ministeri

Sobre

Carreres

Fes-te voluntari

Blog

Premsa

Enllaços útils

Ajuda

Fer un donatiu

Versions de la Bíblia

Bíblia en àudio

Idiomes de la Bíblia

Verset del dia


Un Ministeri Digital de

Life.Church
Català

©2026 Life.Church / YouVersion

Política de privacitatCondicions d'ús
Programa de divulgació de vulnerabilitats
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest