1
Mateyu 11:28
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
“Idzani kwa Ine, inu nonse otopa ndi olemedwa ndipo Ine ndidzakupatsani mpumulo.
Compara
Explorar Mateyu 11:28
2
Mateyu 11:29
Senzani goli langa ndipo phunzirani kwa Ine, pakuti ndine wofatsa ndi wodzichepetsa. Ndipo inu mudzapeza mpumulo wa miyoyo yanu.
Explorar Mateyu 11:29
3
Mateyu 11:30
Pakuti goli langa ndi losavuta ndipo katundu wanga ndi wopepuka.”
Explorar Mateyu 11:30
4
Mateyu 11:27
“Zinthu zonse zapatsidwa kwa Ine ndi Atate anga. Palibe mmodzi amene adziwa Mwana kupatula Atate ndipo palibe mmodzi amene adziwa Atate kupatula Mwana ndi kwa iwo amene Mwana awasankha kuwawululira.
Explorar Mateyu 11:27
5
Mateyu 11:4-5
Yesu anayankha kuti, “Bwererani ndi kukamuwuza Yohane zimene mwamva ndi kuona. Osaona akuona, olumala akuyenda, akhate akuchiritsidwa, osamva akumva, akufa akuukitsidwa ndipo Uthenga Wabwino ukulalikidwa kwa osauka.
Explorar Mateyu 11:4-5
6
Mateyu 11:15
Iye amene ali ndi makutu amve.
Explorar Mateyu 11:15