Logotip de YouVersion
La BíbliaPlansVídeos
Aconsegueix l'aplicació
Selector d'idiomes
Icona de cerca

Versets bíblics populars de Mateyu 11

1

Mateyu 11:28

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

“Idzani kwa Ine, inu nonse otopa ndi olemedwa ndipo Ine ndidzakupatsani mpumulo.

Compara

Explorar Mateyu 11:28

2

Mateyu 11:29

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Senzani goli langa ndipo phunzirani kwa Ine, pakuti ndine wofatsa ndi wodzichepetsa. Ndipo inu mudzapeza mpumulo wa miyoyo yanu.

Compara

Explorar Mateyu 11:29

3

Mateyu 11:30

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Pakuti goli langa ndi losavuta ndipo katundu wanga ndi wopepuka.”

Compara

Explorar Mateyu 11:30

4

Mateyu 11:27

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

“Zinthu zonse zapatsidwa kwa Ine ndi Atate anga. Palibe mmodzi amene adziwa Mwana kupatula Atate ndipo palibe mmodzi amene adziwa Atate kupatula Mwana ndi kwa iwo amene Mwana awasankha kuwawululira.

Compara

Explorar Mateyu 11:27

5

Mateyu 11:4-5

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Yesu anayankha kuti, “Bwererani ndi kukamuwuza Yohane zimene mwamva ndi kuona. Osaona akuona, olumala akuyenda, akhate akuchiritsidwa, osamva akumva, akufa akuukitsidwa ndipo Uthenga Wabwino ukulalikidwa kwa osauka.

Compara

Explorar Mateyu 11:4-5

6

Mateyu 11:15

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Iye amene ali ndi makutu amve.

Compara

Explorar Mateyu 11:15

Plans de lectura i devocionals gratuïts relacionats amb Mateyu 11

Capítol anterior
Capítol següent
YouVersion

Animant-te i desafiant-te a buscar la intimitat amb Déu cada dia.

Ministeri

Sobre

Carreres

Fes-te voluntari

Blog

Premsa

Enllaços útils

Ajuda

Fer un donatiu

Versions de la Bíblia

Bíblia en àudio

Idiomes de la Bíblia

Verset del dia


Un Ministeri Digital de

Life.Church
Català

©2026 Life.Church / YouVersion

Política de privacitatCondicions d'ús
Programa de divulgació de vulnerabilitats
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest