YouVersion Logo
Search Icon

AROMA 4:20-21

AROMA 4:20-21 BLPB2014

ndipo poyang'anira lonjezo la Mulungu sanagwedezeka chifukwa cha kusakhulupirira, koma analimbika m'chikhulupiriro, napatsa Mulungu ulemu, nakhazikikanso mumtima kuti, chimene Iye analonjeza, anali nayonso mphamvu yakuchichita.

Free Reading Plans and Devotionals related to AROMA 4:20-21