YouVersion Logo
Search Icon

MATEYU 10:32-33

MATEYU 10:32-33 BLPB2014

Chifukwa chake yense amene adzavomereza Ine pamaso pa anthu, Inenso ndidzamvomereza iye pamaso pa Atate wanga wa Kumwamba. Koma yense amene adzandikana Ine pamaso pa anthu, Inenso ndidzamkana iye pamaso pa Atate wanga wa Kumwamba.

Free Reading Plans and Devotionals related to MATEYU 10:32-33