YouVersion Logo
Search Icon

AGALATIYA 4:6-7

AGALATIYA 4:6-7 BLPB2014

Ndipo popeza muli ana, Mulungu anatumiza Mzimu wa Mwana wake alowe m'mitima yathu, wofuula Abba! Atate! Kotero kuti sulinso kapolo, koma mwana; koma ngati mwana, wolowa nyumbanso mwa Mulungu.