YouVersion Logo
Search Icon

AGALATIYA 4:4-5

AGALATIYA 4:4-5 BLPB2014

koma pokwaniridwa nthawi, Mulungu anatuma Mwana wake, wobadwa ndi mkazi, wobadwa wakumvera lamulo, kuti akaombole iwo akumvera lamulo, kuti ife tikalandire umwana.