YouVersion Logo
Search Icon

AEFESO 4:22-24

AEFESO 4:22-24 BLPB2014

kuti muvule, kunena za makhalidwe anu oyamba, munthu wakale, wovunda potsata zilakolako za chinyengo; koma kuti mukonzeke, mukhale atsopano mu mzimu wa mtima wanu, nimuvale munthu watsopano, amene analengedwa monga mwa Mulungu, m'chilungamo, ndi m'chiyero cha choonadi.

Free Reading Plans and Devotionals related to AEFESO 4:22-24