YouVersion Logo
Search Icon

AEFESO 4:14-15

AEFESO 4:14-15 BLPB2014

Kuti tisakhalenso makanda, ogwedezekagwedezeka, natengekatengeka ndi mphepo yonse ya chiphunzitso, ndi tsenga la anthu, ndi kuchenjerera kukatsata chinyengo cha kusocheretsa; koma ndi kuchita zoona mwa chikondi tikakule m'zinthu zonse, kufikira Iye amene ali mutu ndiye Khristu

Free Reading Plans and Devotionals related to AEFESO 4:14-15