YouVersion Logo
Search Icon

1 AKORINTO 7:3-4

1 AKORINTO 7:3-4 BLPB2014

Mwamunayo apereke kwa mkazi mangawa ake; koma modzimodzinso mkazi kwa mwamuna. Mkazi alibe ulamuliro wa pa thupi lake la iye yekha, koma mwamuna ndiye; koma momwemonso mwamuna alibe ulamuliro wa pa thupi la iye yekha, koma mkazi ndiye.

Free Reading Plans and Devotionals related to 1 AKORINTO 7:3-4