YouVersion Logo
Search Icon

1 AKORINTO 2:4-5

1 AKORINTO 2:4-5 BLPB2014

Ndipo mau anga ndi kulalikira kwanga sanakhala ndi mau okopa a nzeru, koma m'chionetso cha Mzimu ndi cha mphamvu; kuti chikhulupiriro chanu chisakhale m'nzeru ya anthu, koma mu mphamvu ya Mulungu.