YouVersion Logo
Search Icon

Zekariya 10:1

Zekariya 10:1 CCL

Pemphani mvula kwa Yehova pa nthawi yamphukira; ndi Yehova amene amapanga mitambo ya mvula. Iye amagwetsa mivumbi ya mvula kwa anthu, ndi kumeretsa mbewu za mʼmunda kwa aliyense.

Free Reading Plans and Devotionals related to Zekariya 10:1