YouVersion Logo
Search Icon

Malaki 3:17-18

Malaki 3:17-18 CCL

Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Anthu amenewo adzakhala anga, tsiku limene Ine ndidzachita izi, adzakhala angaanga. Ndidzawaleka osawalanga monga mmene munthu amachitira chifundo mwana wake amene amamutumikira. Pamenepo mudzaonanso kusiyana pakati pa anthu olungama ndi oyipa, pakati pa amene amatumikira Mulungu ndi amene satumikira Mulungu.”

Video for Malaki 3:17-18

Free Reading Plans and Devotionals related to Malaki 3:17-18