YouVersion Logo
Search Icon

Malaki 2:16

Malaki 2:16 CCL

Yehova Mulungu wa Israeli akuti, “Ndimadana ndi kulekana ukwati. Ndimadana ndi munthu wochita zankhanza zotere kwa mkazi wake,” akutero Yehova Wamphamvuzonse. Choncho tetezani mzimu wanu, ndipo musakhale osakhulupirika.

Free Reading Plans and Devotionals related to Malaki 2:16