YouVersion Logo
Search Icon

Levitiko 10:3

Levitiko 10:3 CCL

Pamenepo Mose anawuza Aaroni kuti, “Pajatu Yehova ananena kuti, “ ‘Kwa iwo amene amandiyandikira ndidzaonetsa ulemerero wanga; pamaso pa anthu onse ndidzalemekezedwa.’ ” Aaroni anakhala chete wosayankhula.

Video for Levitiko 10:3