YouVersion Logo
Search Icon

Yesaya 51:16

Yesaya 51:16 CCL

Ndayika mawu anga mʼkamwa mwanu ndipo ndakuphimbani ndi mthunzi wa dzanja langa. Ine ndimayika pa malo pake zinthu za mlengalenga, ndipo ndinayika maziko a dziko lapansi, ndimawuza anthu a ku Ziyoni kuti, ‘Ndinu anthu anga.’ ”

Free Reading Plans and Devotionals related to Yesaya 51:16