YouVersion Logo
Search Icon

Yesaya 45:5-6

Yesaya 45:5-6 CCL

Ine ndine Yehova ndipo palibenso wina; kupatula Ine palibenso Mulungu wina. Ndidzakupatsa mphamvu, ngakhale sukundidziwa Ine, kotero kuti kuchokera kummawa mpaka kumadzulo anthu adzadziwa kuti palibe wina koma Ine ndekha. Ine ndine Yehova, ndipo palibenso wina.

Free Reading Plans and Devotionals related to Yesaya 45:5-6