1
NAHUMU 3:1
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Tsoka mudzi wa mwazi! Udzala nao mabodza ndi zachifwamba; zachifwamba sizidukiza.
Compare
Explore NAHUMU 3:1
2
NAHUMU 3:19
Palibe chakulunzitsa kuthyoka kwako; bala lako liwawa; onse akumva mbiri yako akuombera manja; pakuti ndaniyo kuipa kwako sikunampitapitabe?
Explore NAHUMU 3:19
3
NAHUMU 3:7
Ndipo kudzali kuti onse akupenyerera iwe adzakuthawa, nadzati, Ninive wapasuka, adzamlira maliro ndani? Ndidzakufunira kuti akukutonthoza?
Explore NAHUMU 3:7
Home
Bible
Plans
Videos