1
LEVITIKO 23:3
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Masiku asanu ndi limodzi azigwira ntchito; koma lachisanu ndi chiwiri ndilo Sabata lakupumula, msonkhano wopatulika; musamagwira ntchito konse; ndilo Sabata la Yehova m'nyumba zanu zonse.
Compare
Explore LEVITIKO 23:3
Home
Bible
Plans
Videos