1
LEVITIKO 20:13
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Munthu akagonana ndi mwamuna mnzake, monga amagonana ndi mkazi, achita chonyansa onse awiri; awaphe ndithu; mwazi wao ukhale pamtu pao.
Compare
Explore LEVITIKO 20:13
2
LEVITIKO 20:7
Chifukwa chake dzipatuleni, nimukhale oyera; pakuti Ine ndine Yehova Mulungu wanu.
Explore LEVITIKO 20:7
3
LEVITIKO 20:26
Ndipo muzikhala oyera kwa Ine; pakuti Ine Yehova ndine woyera, ndipo ndinakusiyanitsani kwa mitundu ya anthu mukhale anga.
Explore LEVITIKO 20:26
4
LEVITIKO 20:8
Ndipo musunge malemba anga ndi kuwachita; Ine ndine Yehova wakupatula inu.
Explore LEVITIKO 20:8
Home
Bible
Plans
Videos