1
LEVITIKO 18:22
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Usamagonana ndi mwamuna, monga amagonana ndi mkazi; chonyansa ichi.
Compare
Explore LEVITIKO 18:22
2
LEVITIKO 18:23
Ndipo usamagonana ndi nyama iliyonse, kudetsedwa nayo; kapena mkazi asamaima panyama, kugonana nayo; chisokonezo choopsa ichi.
Explore LEVITIKO 18:23
3
LEVITIKO 18:21
Ndipo usamapereka a mbumba yako kuwapitiriza kumoto chifukwa cha Moleki; usamaipsa dzina la Mulungu wako; Ine ndine Yehova.
Explore LEVITIKO 18:21
Home
Bible
Plans
Videos