1
Zekariya 10:1
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Pemphani mvula kwa Yehova pa nthawi yamphukira; ndi Yehova amene amapanga mitambo ya mvula. Iye amagwetsa mivumbi ya mvula kwa anthu, ndi kumeretsa mbewu za mʼmunda kwa aliyense.
Compare
Explore Zekariya 10:1
2
Zekariya 10:12
Ndidzalimbitsa iwo mwa Yehova ndipo adzayenda mʼdzina lake,” akutero Yehova.
Explore Zekariya 10:12