1
Levitiko 6:13
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Moto uzikhala ukuyaka pa guwa nthawi zonse ndipo usazimepo.
Compare
Explore Levitiko 6:13
2
Levitiko 6:12
Moto wa pa guwa uzikhala ukuyaka nthawi zonse, usamazime. Mmawa uliwonse wansembe aziwonjezerapo nkhuni pa motopo ndi kukonza nsembe yopsereza, ndi kutentha mafuta a nsembe yachiyanjano pamenepo.
Explore Levitiko 6:12