1
Levitiko 11:45
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Ine ndine Yehova amene ndinakutulutsani ku Igupto kuti ndikhale Mulungu wanu. Tsono mukhale woyera, chifukwa Ine ndine woyera.
Compare
Explore Levitiko 11:45
2
Levitiko 11:44
Ine ndine Yehova Mulungu wanu, choncho dziyeretseni kuti mukhale woyera, chifukwa Ine ndine woyera. Musadzisandutse odetsedwa ndi chokwawa chilichonse.
Explore Levitiko 11:44